Proverbs 12:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ogwira ntchito mwakhama adzakhala olamulira, koma aulesi adzakhala akapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Dzanja la akhama lidzalamulira; koma waulesi adzakhala ngati kapolo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ogwira ntchito mwakhama adzalamulira, koma aulesi adzakhala ngati kapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Dzanja la akhama lidzalamulira; Koma wolesi adzakhala ngati kapolo,