Proverbs 12:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nkhaŵa ya munthu imakhala ngati katundu wolemera mumtima mwake, koma mau abwino amamsangalatsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nkhawa iweramitsa mtima wa munthu; koma mau abwino aukondweretsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nkhawa imakhala ngati katundu wolemera mu mtima mwa munthu, koma mawu abwino amamusangalatsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nkhawa iweramitsa mtima wa munthu; Koma mau abwino aukondweretsa.