Proverbs 12:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wochita zabwino amatsogolera anzake pa njira yokhoza, koma njira ya munthu woipa imaŵasokeretsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wolungama atsogolera mnzake; koma njira ya oipa iwasokeretsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wolungama amatsogolera mnansi wake, koma ntchito za anthu oyipa zimawasocheretsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolungama atsogolera mnzace; Koma njira ya oipa iwasokeretsa.