Proverbs 12:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Njira ya chilungamo imafikitsa ku moyo, koma njira ya zoipa imafikitsa ku imfa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'khwalala la chilungamo muli moyo; m'njira ya mayendedwe ake mulibe imfa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼnjira yachilungamo muli moyo; koma njira ya munthu woyipa imafikitsa ku imfa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'khwalala la cilungamo muli moyo; M'njira ya mayendedwe ace mulibe imfa.