Proverbs 12:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu sakhazikika bwino pochita uchimo, koma maziko a munthu wochita zabwino sadzagwedezeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu sadzakhazikika ndi udyo, muzu wa olungama sudzasunthidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu sangakhazikike bwino pochita zoyipa, koma maziko a anthu olungama sadzatekeseka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu sadzakhazikika ndi udio, Muzu wa olungama sudzasunthidwa.