Proverbs 12:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maganizo a munthu wabwino ngoongoka, koma malangizo a munthu woipa ngonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maganizo a olungama ndi chiweruzo; koma uphungu wa oipa unyenga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maganizo a anthu olungama ndi owongoka, koma malangizo a anthu oyipa ndi achinyengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maganizo a olungama ndi ciweruzo; Koma uphungu wa oipa unyenga.