Proverbs 12:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a munthu woipa mtima ngophetsa, koma mau a munthu wolungama ngopulumutsa anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau a oipa abisalira mwazi; koma m'kamwa mwa olungama muwalanditsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu a anthu oyipa ndi ophetsa, koma mawu a anthu olungama amapulumutsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau a oipa abisalira mwazi; Koma m'kamwa mwa olungama muwalanditsa.