Proverbs 12:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu oipa mtima amagwetsedwa, naiŵalika, koma banja la anthu omvera Mulungu silidzapasuka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Oipa amagwa kuli zii; koma banja la olungama limaimabe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu oyipa amagonjetsedwa ndipo amayiwalika, koma nyumba ya anthu olungama idzakhalabe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Oipa amagwa kuli zi; Koma banja la olungama limaimabe.