Proverbs 12:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amamuyamika malinga ndi nzeru zake, koma munthu wa mtima wokhota amanyozeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu amatamandidwa monga mwa nzeru yake; koma wokhota mtima adzanyozedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amatamandidwa malinga ndi nzeru zake, koma anthu amitima yokhota amanyozedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu amatamandidwa monga mwa nzeru yace; Koma wokhota mtima adzanyozedwa.