Proverbs 12:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wamba, wodzigwirira ntchito napeza zofunika, ali pabwino kuposa wongodzikuza, pamene alibe nchakudya chomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wonyozedwa, amene ali ndi kapolo, aposa wodzikuza, amene asowa zakudya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkwabwino kukhala munthu wonyozeka koma wodzigwirira ntchito nʼkukhala ndi zonse zofunika, kuposa kukhala wodzikuza koma ulibe ndi chakudya chomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wonyozedwa, amene ali ndi kapolo, Aposa wodzikuza, amene asowa zakudya.