Proverbs 13:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woyenda ndi anthu anzeru nayenso amakhala ndi nzeru, koma woyenda ndi zitsiru adzaonongeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukayenda ndi anzeru udzakhala wanzeru: koma mnzao wa opusa adzaphwetekedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Woyenda ndi anthu anzeru nayenso adzakhala wanzeru; koma woyenda ndi zitsiru adzapwetekeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukayenda ndi anzeru udzakhala wanzeru: Koma mnzao wa opusa adzaphwetekedwa.