Proverbs 13:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene sakwapula mwana wake, ndiye kuti samkonda, koma amene amakonda mwana wake, sazengereza kumlanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wolekerera mwanake osammenya amuda; koma womkonda amyambize kumlanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene sakwapula mwana wake, ndiye kuti amamuda, koma wokonda mwana wake sazengereza kumulanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolekereramwanace osammenya amuda; Koma womkonda amyambize kumlanga.