Proverbs 13:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuŵala kwa anthu a Mulungu kumachita kuti ngwee, koma nyale ya anthu oipa mtima siidzalephera kuzima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuunika kwa olungama kukondwa; koma nyali ya oipa idzazima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyale ya munthu wolungama ndi yokondweretsa, koma nyale ya munthu woyipa imazimitsidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuunika kwa olungama kukondwa; Koma nyali ya oipa idzazima.