Proverbs 14:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mkazi wanzeru amamanga banja lake, koma wopusa amalipasula ndi zochita zake zomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkazi yense wanzeru amanga banja lake; koma wopusa alipasula ndi manja ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mkazi wanzeru amamanga banja lake, koma mkazi wopusa amalimasula ndi manja ake omwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkazi yense wanzeru amanga banja lace; Koma wopusa alipasula ndi manja ace.