Proverbs 14:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyumba ya munthu woipa idzapasuka, koma hema la munthu wolungama lidzakhazikika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nyumba ya oipa idzapasuka; koma hema wa oongoka mtima adzakula.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyumba ya munthu woyipa idzapasuka, koma tenti ya munthu wowongoka mtima idzakhazikika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nyumba ya oipa idzapasuka; Koma hema wa oongoka mtima adzakula.