Proverbs 14:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu, koma kopherezera kwake nku imfa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ilipo njira yooneka kwa mwamuna ngati yoongoka; koma matsiriziro ake ndi njira za imfa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu, koma kumatsiriziro kwake ndi ku imfa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iripo njira yooneka kwa mwamuna ngati yoongoka; Koma matsiriziro ace ndi njira za imfa.