Proverbs 14:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wanzeru ngwochenjera, ndipo amalewa choipa, koma chitsiru chimadudukira zinthu mosasamalako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wanzeru amaopa nasiya zoipa; koma wopusa amanyada osatekeseka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wanzeru amaopa Mulungu ndipo amapewa zoyipa, koma munthu wopusa ndi wokula mtima amakhala wosasamala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wanzeru amaopa nasiya zoipa; Koma wopusa amanyada osatekeseka.