Proverbs 14:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wopsa mtima msanga amachita zauchitsiru, wa khalidwe lonyenga, anthu amadana naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokangaza kukwiya adzachita utsiru; ndipo munthu wa ziwembu adzadedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wopsa mtima msanga amachita zinthu za uchitsiru, ndipo anthu amadana ndi munthu wachinyengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokangaza kukwiya adzacita utsiru; Ndipo munthu wa ziwembu adzadedwa.