Proverbs 14:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu opusa wao ndi uchitsiru, koma ochenjera yao ndi mphotho ya kudziŵa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Achibwana amalandira cholowa cha utsiru; koma ochenjera amavala nzeru ngati korona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu opusa amalandira uchitsiru, koma anthu ochenjera amavekedwa chipewa cha ulemerero wa kudziwa zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Acibwana amalandira colowa ca utsiru; Koma ocenjera amabvala nzeru ngati korona.