Proverbs 14:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amanyoza mnzake ngwochimwa, koma ngwodala amene amachitira chifundo amphaŵi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wonyoza anzake achimwa; koma wochitira osauka chifundo adala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wonyoza mnansi wake ndi wochimwa koma ndi wodala amene amachitira chifundo anthu osowa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wonyoza anzace acimwa; Koma wocitira osauka cifundo adala.