Proverbs 14:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi amene amakonzekera zoipa sachimwa? Koma amene amakonzekera zabwino anthu amaŵaonetsa chifundo ndi kukhulupirika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi oganizira zoipa sasochera? Koma akuganizira zabwino adzalandira chifundo ndi ntheradi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi amene amakonzekera zoyipa sasochera? Koma amene amakonzekera zabwino anthu amawaonetsa chikondi ndi kukhulupirika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi oganizira zoipa sasocera? Koma akuganizira zabwino adzalandira cifundo ndi ntheradi.