Proverbs 14:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa ntchito iliyonse pali phindu lake, koma kumangolakatika kumabweretsa umphaŵi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'ntchito zonse muli phindu; koma kulankhulalankhula kungopatsa umphawi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ntchito iliyonse imakhala ndi phindu, koma kuyankhulayankhula kumabweretsa umphawi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'nchito zonse muli phindu; Koma kulankhula-lankhula kungopatsa umphawi.