Proverbs 14:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mphotho ya anthu anzeru ndi nzeru zao zomwe, koma anthu opusa malipiro ao ndi uchitsiru wao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Korona wa anzeru ndi chuma chao; utsiru wa opusa ndiwo utsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chipewa chaulemu cha anthu a nzeru ndi chuma chawo chomwe, koma malipiro a zitsiru ndi uchitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Korona wa anzeru ndi cuma cao; Utsiru wa opusa ndiwo utsiru.