Proverbs 14:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chinamtindi cha anthu ndiye ulemerero wake wa mfumu, koma anthu akasoŵa, ufumu wake umasanduka wachabechabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mu unyinji wa anthu muli ulemu wa mfumu; koma popanda anthu kalonga aonongeka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Gulu lalikulu la anthu ndiye ulemerero wa mfumu, koma popanda anthu kalonga amawonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mu unyinji wa anthu muli ulemu wa mfumu; Koma popanda anthu kalonga aonongeka.