Proverbs 14:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wosapsa mtima msanga amamvetsa zinthu kwambiri, koma wofulumira kupsa mtima amaonetsa uchitsiru wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wosakwiya msanga apambana kumvetsa; koma wansontho akuza utsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wosapsa mtima msanga amamvetsa zinthu kwambiri, koma munthu wopsa mtima msanga amaonetsa uchitsiru wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wosakwiya msanga apambana kumvetsa; Koma wansontho akuza utsiru.