Proverbs 14:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kulankhula kwa chitsiru kumamuitanira ndodo pa msana, koma mau a munthu wanzeru amamteteza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kamwa mwa chitsiru muli nthyole ya kudzikuza; koma milomo ya anzeru idzawasunga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuyankhula kwa chitsiru kumamuyitanira ndodo pa msana, koma milomo ya munthu wanzeru imamuteteza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kamwa mwa citsiru muli ntyole ya kudzikuza; Koma milomo ya anzeru Idzawasunga.