Proverbs 14:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu ochita zoipa amatayika, koma ochita zabwino amatetezedwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wochimwa adzakankhidwa m'kuipa kwake; koma wolungama akhulupirirabe pomwalira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu oyipa adzakanthidwa chifukwa cha ntchito zawo zomwe, koma olungama adzatetezedwa mwa imfa yawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wocimwa adzakankhidwa m'kuipa kwace; Koma wolungama akhulupirirabe pomwalira,