Proverbs 14:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nzeru zimakhala mumtima mwa anthu omvetsa zinthu, koma mumtima mwa zitsiru sizipezeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru ikhalabe m'mtima wa wozindikira, nidziwika pakati pa opusa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nzeru zimakhala mu mtima mwa anthu omvetsa zinthu, koma nzeru sipezeka mu mtima mwa zitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru ikhalabe m'mtima wa wozindikira, Nidziwika pakati pa opusa.