Proverbs 14:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mfumu imakondwa ndi mtumiki wochita zinthu mwanzeru, koma imakwiyira wochita zinthu mochititsa manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mfumu ikomera mtima kapolo wochita mwanzeru; koma idzakwiyira wochititsa manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu imasangalatsidwa ndi wantchito wanzeru, koma imachitira ukali wantchito wochititsa manyazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mfumu ikomera mtima kapolo wocita mwanzeru; Koma idzakwiyira wocititsa manyazi.