Proverbs 14:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wonyoza anzake amafunafuna nzeru osaipeza, koma munthu womvetsa amadziŵa bwino zinthu msanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wonyoza afunafuna nzeru osaipeza; koma wozindikira saona vuto m'kuphunzira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza, koma munthu womvetsa bwino amadziwa zinthu msanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wonyoza afunafuna nzeru osaipeza; Koma wozindikira saona bvuto m'kuphunzira.