Proverbs 14:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usayandikirepo pamene pali chitsiru, paja pamenepo supezapo mau anzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pita pamaso pa munthu wopusa, sudzazindikira milomo yakudziwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Khala kutali ndi munthu wopusa chifukwa sudzapeza mawu a nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pita pamaso pa munthu wopusa, Sudzazindikira milomo yakudziwa.