Proverbs 14:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nzeru za munthu wochenjera zagona pa kuzindikira bwino njira zake, koma zitsiru zimanyengedwa nkupusa kwao komwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru ya wochenjera ndiyo yakuti azindikire njira yake; koma utsiru wa opusa ndiwo chinyengo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nzeru za munthu wochenjera zagona pakuzindikira njira zake. Koma uchitsiru wa zitsiru umapusitsidwa ndi chinyengo chawo chomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru ya wocenjera ndiyo yakuti azindikire njira yace; Koma utsiru wa opusa ndiwo cinyengo.