Proverbs 14:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zitsiru sizilabadako za kulapa machimo ao, kufuna kwabwino kumapezeka mwa anthu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zitsiru zinyoza kupalamula; koma mwa oongoka mtima muli chiyanjano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zitsiru zimanyoza za kulapa machimo, awo, koma kufuna kwabwino kumapezeka mwa anthu olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zitsiru zinyoza kuparamula; Koma mwa oongoka mtima muli ciyanjano.