Proverbs 15:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wopsa mtima msanga amautsa mkangano, koma munthu woleza mtima amabweretsa mtendere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu wozaza aputa makani; koma wosakwiya msanga atonthoza makangano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano, koma munthu woleza mtima amathetsa ndewu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu wozaza aputa makani; Koma wosakwiya msanga atonthoza makangano.