Proverbs 16:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuchita zoipa kumanyansa mafumu, pakuti chilungamo ndiye maziko a ufumu wao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuchita mphulupulu kunyansa mafumu; pakuti mpando wao wakhazikika ndi chilungamo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuchita zoyipa kumanyansa mafumu, pakuti chilungamo ndiye maziko a ufumu wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kucita mphulupulu kunyansa mafumu; Pakuti mpando wao wakhazikika ndi cilungamo.