Proverbs 16:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mfumu ikakwiya, ndiye kuti imfa ili pafupi, koma munthu wanzeru amaupepesa mkwiyowo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkwiyo wa mfumu ndi mithenga ya imfa; wanzeru adzaukhulula.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ukali wa mfumu ndi mthenga wa imfa, koma munthu wanzeru amawupepesa ukaliwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkwiyo wa mfumu ndi mithenga ya imfa; Wanzeru adzaukhulula.