Proverbs 16:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kukoma mtima kwa mfumu kumadzetsa moyo, kuli ngati mitambo ya mvula yam'chilimwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kuunika kwa nkhope ya mfumu muli moyo; kukoma mtima kwake kunga mtambo wa mvula ya masika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuwala kwa nkhope ya mfumu kumapatsa moyo; ndipo kukoma mtima kwake kuli ngati mitambo ya mvula nthawi ya chilimwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kuunika kwa nkhope ya mfumu muli moyo; Kukoma mtima kwace kunga mtambo wa mvula ya masika.