Proverbs 16:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kunyada kumafikitsa ku chiwonongeko, ndipo munthu wa mtima wodzikuza adzagwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kunyada kutsogolera kuonongeka; mtima wodzikuza ndi kutsogolera kuphunthwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kunyada kumafikitsa ku chiwonongeko, ndipo munthu wodzikuza adzagwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kunyada kutsogolera kuonongeka Mtinia wodzikuza ndi kutsogolera kupunthwa.