Proverbs 16:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuli bwino kukhala ndi mtima wodzichepetsa pakati pa anthu osauka, kupambana kumagaŵana chuma ndi anthu onyada.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kufatsa mtima ndi osauka kuposa kugawana zofunkha ndi onyada.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkwabwino kukhala ndi mtima wodzichepetsa pakati pa anthu oponderezedwa, kusiyana ndi kugawana zolanda ndi anthu onyada.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kufatsa mtima ndi osauka Kuposa kugawana zofunkha ndi onyada.