Proverbs 16:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nzeru ndi kasupe wopatsa moyo kwa amene ali nazo, koma uchitsiru umabweretsa chilango kwa anthu opusa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru ndi kasupe wa moyo kwa mwini wake; koma mwambo wa zitsiru ndi utsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumvetsa zinthu ndi kasupe wa moyo kwa iwo amene ali nako, koma uchitsiru umabweretsa chilango kwa zitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru ndi kasupe wa moyo kwa mwini wace; Koma mwambo wa zitsiru ndi utsiru.