Proverbs 16:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wa munthu wanzeru umamlankhulitsa mau ochenjera, nzeruzo zimakulitsa mphamvu ya mau ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa wanzeru uchenjeza m'kamwa mwake, nuphunzitsanso milomo yake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wanzeru umathandiza munthu kuyankhula mwa nzeru, ndipo mawu ake amawonjezera nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa wanzeru ucenjeza m'kamwa mwace, Nuphunzitsanso milomo yace.