Proverbs 16:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamakhala njira ina yooneka yowongoka kwa munthu, koma kumapeto kwake imakhala njira ya ku imfa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ilipo njira yooneka kwa mwamuna ngati yoongoka, koma matsiriziro ake ndi njira za imfa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pali njira ina yooneka ngati yowongoka kwa munthu koma kumatsiriziro kwake ndi imfa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iripo njira yooneka kwa mwamuna ngati yoongoka, Koma matsiriziro ace ndi njira za imfa.