Proverbs 16:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Njala ya munthu wantchito imamthandiza kulimbikira, ndi njalayo imene imamkakamiza kuchita kanthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wantchito adzigwirira yekha ntchito; pakuti m'kamwa mwake mumfulumiza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Njala ya munthu wantchito imamuthandiza kulimbikira; njalayo imamukakamiza kuchitapo kanthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wanchito adzigwirira yekha nchito; Pakuti m'kamwa mwace mumfulumiza.