Proverbs 16:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu woipa mtima amafalitsa mkangano, kazitape amadanitsa anthu okhala pa chibwenzibwenzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu wokhota amautsa makani; kazitape afetsa ubwenzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa mtima amayambitsa mikangano, ndipo miseche imalekanitsa anthu okondana kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu wokhota amautsa makani; Kazitape afetsa ubwenzi.