Proverbs 16:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wosapsa mtima msanga amapambana wankhondo, amene amadzigwira mtima amapambana msilikali wogonjetsa mzinda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wosakwiya msanga aposa wamphamvu; wolamulira mtima wake naposa wolanda mudzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wosapsa mtima msanga amaposa munthu wankhondo, munthu wowugwira mtima wake amaposa amene amalanda mzinda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wosakwiya msanga aposa wamphamvu; Wolamulira mtima wace naposa wolanda mudzi.