Proverbs 16:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adapanga chinthu chilichonse kuti chikhale ndi cholinga chake, ngakhale anthu oipa, kuti aone tsiku la mavuto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zonse Yehova anazipanga zili ndi zifukwa zao; ngakhale amphulupulu kuti aone tsiku loipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova amachita zonse ndi cholinga chake, ngakhale anthu oyipa kuti aone tsiku latsoka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zonse Yehova anazipangaziri ndi zifukwa zao; Ngakhale amphulupulu kuti aone tsiku loipa,