Proverbs 16:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuli bwino kukhala ndi zinthu pang'ono uli ndi chilungamo kupambana kukhala ndi chuma chambirimbiri ulibe chilungamo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zapang'ono, pokhala chilungamo, ziposa phindu lalikulu lopanda chiweruzo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono zozipeza mwachilungamo, kusiyana ndi kukhala ndi zinthu zambiri zozipeza popanda chilungamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zapang'ono, pokhala cilungamo, Ziposa phindu lalikuru lopanda ciweruzo.