Proverbs 16:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wa munthu umalingalira zoti uchite, koma Chauta ndiye amene amaongolera mayendedwe a munthuyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa munthu ulingalira njira yake; koma Yehova ayendetsa mapazi ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wa munthu umalingalira zochita, koma Yehova ndiye amakhazikitsa njira zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa munthu ulingalira njira yace; Koma Yehova ayendetsa mapazi ace.