Proverbs 17:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu woipa mtima amangofuna zoukira. Tsono adzamtumira wamthenga wankhalwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Woipa amafuna kupanduka kokha; koma adzamtumizira mthenga wankhanza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa maganizo ake ali pa kuwukira basi; ndipo bwana adzamutumizira wamthenga wankhanza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Woipa amafuna kupanduka kokha; Koma adzamtumizira mthenga wankhanza.