Proverbs 17:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chiyambi cha mkangano chili ngati kukhamulira madzi, ndiye uzichokapo ndeu isanabuke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chiyambi cha ndeu chifanana ndi kutsegulira madzi; tsono kupikisana kusanayambe tasiya makani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiyambi cha mikangano chili ngati kukhamulira madzi, choncho uzichokapo mkangano usanayambe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ciyambi ca ndeu cifanana ndi kutsegulira madzi; Tsono kupikisana kusanayambe tasiya makani.